Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 March tsamba 6
  • Yobu Sankakayikira Kuti Akufa Adzauka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yobu Sankakayikira Kuti Akufa Adzauka
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Mtengo Ukadulidwa Umaphukanso?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Mtengo Wauŵisi wa Azitona M’nyumba ya Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2000
  • ‘Nzeru za Mulungu N’zozama’ Kwambiri
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Fanizo la Mtengo wa Maolivi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 March tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOBU 11-15

Yobu Sankakayikira Kuti Akufa Adzauka

Yobu anasonyeza kuti ankakhulupirira kuti Mulungu adzamuukitsa

14:7-9, 13-15

Chitsa chouma cha mtengo wa maolivi chikuphukiranso
  • Yobu anagwiritsa ntchito chitsanzo cha mtengo, mwina wa maolivi, pofuna kusonyeza chikhulupiriro chimene anali nacho chakuti Mulungu angathe kumuukitsa

  • Mizu ya mtengo wa maolivi imakhala yambiri komanso imakafika patali. Zimenezi zimachititsa kuti chitsa chake chiziphukirabe ngakhale thunthu lake litadulidwa

  • Ngakhale kutachita chilala mpaka chitsa cha mtengowu kuuma, kukagwa mvula, nthambi zina zimaphukiranso kuchokera ku mizu yake

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena