Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Pezani Nzeru Ndipo Landirani Mwambo
    Nsanja ya Olonda—1999 | September 15
    • Mawu oyamba a buku la Miyambo, afotokoza cholinga chenicheni cha bukuli: “Miyambo ya Solomo mwana wa Davide, mfumu ya Israyeli. Kudziŵa nzeru ndi mwambo; kuzindikira mawu ozindikiritsa; kulandira mwambo wakusamalira machitidwe, chilungamo, chiweruzo ndi zolunjika; kuchenjeza achibwana, kuphunzitsa mnyamata kudziŵa ndi kulingalira.”​—Miyambo 1:1-4.

  • Pezani Nzeru Ndipo Landirani Mwambo
    Nsanja ya Olonda—1999 | September 15
    • Nzeru imaphatikiza mbali zambiri monga kumvetsa, chidziŵitso, kuchenjera, ndi luso la kulingalira. Kumvetsa ndiko kukhoza kuona chimene nkhaniyo ikutanthauza ndi kuzindikira nkhani yonseyo mwa kumvetsa kugwirizana kwa mbali zake zonse ndi mutu wa nkhaniyo, potero mukumamvetsa tanthauzo lake. Chidziŵitso chimafuna kudziŵa ndi kumvetsa chifukwa chake kuchita zinthu zina zake n’kwabwino kapena ayi. Mwachitsanzo, munthu womvetsa angazindikire pamene winawake akufuna kulakwa, ndipo nthaŵi yomweyo angam’chenjeze za kuwopsa kwa chomwe akufuna kuchitacho. Koma adzafunikira chidziŵitso kuti azindikire chifukwa chake munthu ameneyo akuchitira zimenezo kuti athe kupeza njira yabwino yom’pulumutsira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena