Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mfundo Zazikulu za Nyimbo ya Solomo
    Nsanja ya Olonda—2006 | November 15
    • 1:2, 3​—N’chifukwa chiyani kukumbukira chikondi cha m’busayo kukufanana ndi vinyo ndiponso dzina lake likunga mafuta? Monga mmene vinyo amakondweretsera mtima wa munthu, ndi mmene mafuta amaziziritsira tikawadzola pa mutu, kukumbukira chikondi cha mnyamatayo ndiponso dzina lake kunalimbikitsa ndi kutonthoza namwaliyo. (Salmo 23:5; 104:15) Akhristu oona, makamaka odzozedwa, amapeza mphamvu ndiponso amalimbikitsidwa akamaganizira za chikondi chimene Yesu Khristu wawasonyeza.

  • Mfundo Zazikulu za Nyimbo ya Solomo
    Nsanja ya Olonda—2006 | November 15
    • 1:2; 2:6. Mawu ndi zochita zabwino zosonyeza chikondi zingakhale zoyenera pamene tili pachibwenzi. Komabe, mwamuna ndi mkazi ayenera kusamala kuti chimenechi chizikhala chikondi chenicheni osati chilakolako chonyansa, chimene chingawachititse chisembwere.​—Agalatiya 5:19.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena