Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsamba 6
  • Yehova Amapereka Mphamvu kwa Munthu Wotopa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amapereka Mphamvu kwa Munthu Wotopa
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Kuuluka Pamwamba ndi Mapiko Monga Ziombankhanga
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Maso a Chiwombankhanga
    Galamukani!—2003
  • Zimene Tingaphunzire kwa Mbalame
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
  • Zinyama Zimalemekeza Yehova
    Nsanja ya Olonda—2006
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 January tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YESAYA 38-42

Yehova Amapereka Mphamvu kwa Munthu Wotopa

40:29-31

  • Chiwombankhanga chikhoza kuuluka nthawi yaitali pogwiritsa ntchito mpweya wotentha. Chikafika pamene pakuwomba mpweyawu chimauluka mozungulira pamwamba pa mpweyawo ndipo chimakankhidwa mpaka kupita m’mwamba. Chikafika m’mwambamo, chimafufuza pomwe pali mpweya wina wotentha womwe umachikankhanso mpaka m’mwamba kwambiri

  • Zimene zimachitika kuti chiwombankhanga chizitha kuuluka kwa nthawi yaitali zikufanana ndi mmene Yehova amatipatsira mphamvu kuti tisatope pomutumikira

Chiwombankhanga chimauluka nthawi yaitali pogwiritsa ntchito mpweya wotentha
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena