Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsamba 3
  • “Mfumu Idzalamulira Mwachilungamo”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mfumu Idzalamulira Mwachilungamo”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • “Mukhale Tcheru ndi Kuyang’anira Gulu Lonse la Nkhosa”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • “Wetani Gulu la Nkhosa za Mulungu Lomwe Analisiya M’manja Mwanu”
    Nsanja ya Olonda—2011
  • “Wetani Gulu la Mulungu”
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Musawopa, Kagulu ka Nkhosa Inu”
    Nsanja ya Olonda—1995
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 January tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YESAYA 29-33

“Mfumu Idzalamulira Mwachilungamo”

Yesu, yemwe ndi Mfumu, amapereka “akalonga” kapena kuti akulu amene amasamalira nkhosa

32:1-3

  • Mofanana ndi “malo ousapo mvula yamkuntho,” iwo amayesetsa kuteteza nkhosa ngati zikuzunzidwa komanso amazilimbikitsa zikafooka

  • Mofanana ndi “mitsinje yamadzi m’dziko lopanda madzi,” iwo amatsitsimula nkhosa zimene zili ndi ludzu poziphunzitsa mfundo zolondola za choonadi

  • Mofanana ndi “mthunzi wa thanthwe lalikulu m’dziko louma,” iwo amatonthoza nkhosa pozipatsa malangizo olimbikitsa a m’Baibulo

    Munthu wabisala nthawi ya mvula, akumwa madzi mumtsinje, ndiponso akupuma pa mthunzi wa thanthwe
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena