Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani Zokhudza Danieli?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Zomwe Danieli analemba: Nebukadinezara anaimika fano lalikulu ndipo analamula anthu kuti azililambira. Wina akakana kuchita zimenezi, ankamuponya mung’anjo yoyaka moto.—Danieli 3:1-6.

  • Kodi Baibulo Limanena Zotani Zokhudza Danieli?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Ponena zoponya anthu mung’anjo yamoto, mbiri ya mzinda wa wakale wa Babulo, imafotokoza za nkhaniyi mobwerezabwereza. Mbiriyi imafotokozanso za anthu ena omwe analandira chilangochi pambuyo poti mfumu yapereka chilolezo. Munkhani ina yakale yomwe inalembedwa m’nthawi ya ulamuliro wa Mfumu Nebukadinezara, inafotokoza za chilango chomwe akuluakulu ena aboma anapatsidwa chifukwa chonyoza milungu ya ku Babulo. Nkhaniyo imati: “ Awonongeni, awotcheni, awambeni . . . mu uvuni . . . afuke utsi, moto wawo ulilime kwambiri ndipo pafuke utsi wambiri kuti asakhalenso ndi moyo.”a

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena