Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Pali Munthu Amene Anaonapo Mulungu?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Masomphenya.

      Mulungu ankaonekera kwa anthu kudzera m’masomphenya, kapena kuti zinthu zimene anthuwo ankaona m’maganizo mwawo. Mwachitsanzo, Baibulo likamanena kuti Mose ndi Aisiraeli “anaona Mulungu wa Isiraeli,” limatanthauza kuti “iwo anaona masomphenya a Mulungu woona.” (Ekisodo 24:9-11) Mofanana ndi zimenezi nthawi zina Baibulo limanena kuti aneneri ‘ankaona Yehova.’ (Yesaya 6:1; Danieli 7:9; Amosi 9:1) Nkhani zonsezi zikusonyezeratu kuti anthuwo sankaona Mulungu weniweni koma ankangoona masomphenya.​—Yesaya 1:1; Danieli 7:2; Amosi 1:1.

  • Kodi Mulungu Ali ndi Mayina Angati?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Wamasiku Ambiri

      Danieli 7:9, 13, 22

      Mulungu alibe chiyambi. Iye wakhala alipo kuyambira kalekale munthu aliyense komanso chinthu chilichonse zisanapangidwe.​—Salimo 90:2.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena