Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2012 | June 15
    • ▪ Chifaniziro chachikulu chimene Mfumu Nebukadinezara inalota sichiimira maulamuliro onse amphamvu apadzikoli. (Dan. 2:31-45) Chimangoimira maulamuliro asanu amene analamulira kuyambira nthawi ya Danieli, omwe analowerera kwambiri pa zochita za anthu a Mulungu.

  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2012 | June 15
    • a Ulamuliro wa Britain ndi America uli ngati chitsulo. Koma dongo limene linasakanizidwa ndi chitsulocho likuimira zinthu zimene anthu ena amene ali pansi pa ulamulirowu akuchita. Dongoli lakhala likuchititsa kuti ulamulirowu usakhale wamphamvu kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena