-
Mafunso Ochokera kwa OwerengaNsanja ya Olonda—2012 | June 15
-
-
▪ Chifaniziro chachikulu chimene Mfumu Nebukadinezara inalota sichiimira maulamuliro onse amphamvu apadzikoli. (Dan. 2:31-45) Chimangoimira maulamuliro asanu amene analamulira kuyambira nthawi ya Danieli, omwe analowerera kwambiri pa zochita za anthu a Mulungu.
-
-
Mafunso Ochokera kwa OwerengaNsanja ya Olonda—2012 | June 15
-
-
a Ulamuliro wa Britain ndi America uli ngati chitsulo. Koma dongo limene linasakanizidwa ndi chitsulocho likuimira zinthu zimene anthu ena amene ali pansi pa ulamulirowu akuchita. Dongoli lakhala likuchititsa kuti ulamulirowu usakhale wamphamvu kwambiri.
-