Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 November tsamba 6
  • Khalanibe Maso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalanibe Maso
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Oipa Adzakhalabe kwa Utali Wotani?
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Muzikhulupirira Yehova Kuti Mukhale ndi Moyo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Tengerani Chitsanzo kwa Aneneri—Habakuku
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Mfundo Zazikulu za M’mabuku a Nahumu, Habakuku, ndi Zefaniya
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 November tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | NAHUMU 1–HABAKUKU 3

Khalanibe Maso

Hab. 1:5, 6

Zinali zosayembekezereka kuti Ababulo angawononge mzinda wa Yuda. Ayuda ankathandizidwa ndi Aiguputo omwe anali amphamvu kwambiri kuposa Ababulo. Kuwonjezera apo, Ayuda ambiri ankaona kuti Yehova sangalole kuti Yerusalemu ndi kachisi ziwonongedwe. Komabe ulosi unkayenera kukwaniritsidwa ndithu ndipo Habakuku ankafunika kukhalabe maso pouyembekezera.

Habakuku anakhalabe maso ngakhale kuti panali anthu ambiri amene ankachita zoipa

Kodi n’chiyani chikunditsimikizira kuti mapeto a dzikoli ali pafupi kwambiri?

Kodi ndingatani kuti ndikhalebe maso?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena