Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ulosi wa Yesaya Unakwaniritsidwa
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
    • Ulosi wake unali wakuti: “Taonani mtumiki wanga amene ndamusankha, wokondedwa wanga, amene moyo wanga ukukondwera naye. Ndidzaika mzimu wanga pa iye, ndipo adzasonyeza bwinobwino chilungamo chenicheni kwa anthu a mitundu ina. Sadzakangana ndi munthu, kapena kufuula, ndipo palibe amene adzamva mawu ake m’misewu. Bango lophwanyika sadzalisansantha ndipo nyale yofuka sadzaizimitsa, kufikira atakwanitsa kubweretsa chilungamo. Ndithudi, m’dzina lake mitundu ya anthu idzayembekezera zabwino.”—Mateyu 12:18-21; Yesaya 42:1-4.

  • Ulosi wa Yesaya Unakwaniritsidwa
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
    • Komanso Yesu ankapereka uthenga wotonthoza kwa anthu amene anali ngati bango lophwanyika, lopindika komanso lothyoka. Anthuwa analinso ngati chingwe cha nyale chomwe chatsala pang’ono kuzima. Yesu sanasansanthe bango lophwanyika kapena kuzimitsa chingwe cha nyale yofuka. M’malomwake, analimbikitsa anthu odzichepetsa ndipo anachita zimenezi mwachifundo komanso mwachikondi. Pamenepa n’zoonekeratu kuti Yesu ndi yekhayo amene anthu angamudalire kuti adzasintha zinthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena