Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • “Olungama Adzawala Ngwee Ngati Dzuwa”
    Nsanja ya Olonda—2010 | March 15
    • 3. Fotokozani vuto limene munthu wa m’fanizoli anakumana nalo, nanga anati athana nalo bwanji?

      3 Fanizolo limati: “Ufumu wa kumwamba uli ngati munthu amene anafesa mbewu zabwino m’munda wake. Koma anthu ali m’tulo, kunabwera mdani wake ndi kudzafesa udzu [kapena kuti namsongole] m’munda wa tiriguwo, ndi kuchoka. Tsopano mmerawo utakula ndi kutulutsa ngala, udzu nawonso unaonekera. Ndiye kunabwera akapolo a mwini munda nati kwa iye, ‘Mbuye, kodi simunafese mbewu zabwino m’munda wanuwu? Nanga udzuwu wachokeranso kuti?’ Iye anati kwa iwo, ‘Munthu wina wodana nane anachita zimenezi.’ Iwo anati kwa iye, ‘Tsopano kodi mukufuna kuti tipite kukam’zula?’ Iye anati, ‘Ayi; kuopera kuti mwina pozula udzu, mungazule pamodzi ndi tirigu. Zilekeni zonse zikulire pamodzi mpaka nthawi yokolola; ndipo m’nyengo yokolola ndidzauza okololawo kuti, Choyamba sonkhanitsani udzu ndi kuumanga m’mitolo kuti ukatenthedwe, ndipo mukatha mupite kukasonkhanitsa tirigu ndi kumuika m’nkhokwe yanga.’”​—Mat. 13:24-30.

  • “Olungama Adzawala Ngwee Ngati Dzuwa”
    Nsanja ya Olonda—2010 | March 15
    • 3. Fotokozani vuto limene munthu wa m’fanizoli anakumana nalo, nanga anati athana nalo bwanji?

      3 Fanizolo limati: “Ufumu wa kumwamba uli ngati munthu amene anafesa mbewu zabwino m’munda wake. Koma anthu ali m’tulo, kunabwera mdani wake ndi kudzafesa udzu [kapena kuti namsongole] m’munda wa tiriguwo, ndi kuchoka. Tsopano mmerawo utakula ndi kutulutsa ngala, udzu nawonso unaonekera. Ndiye kunabwera akapolo a mwini munda nati kwa iye, ‘Mbuye, kodi simunafese mbewu zabwino m’munda wanuwu? Nanga udzuwu wachokeranso kuti?’ Iye anati kwa iwo, ‘Munthu wina wodana nane anachita zimenezi.’ Iwo anati kwa iye, ‘Tsopano kodi mukufuna kuti tipite kukam’zula?’ Iye anati, ‘Ayi; kuopera kuti mwina pozula udzu, mungazule pamodzi ndi tirigu. Zilekeni zonse zikulire pamodzi mpaka nthawi yokolola; ndipo m’nyengo yokolola ndidzauza okololawo kuti, Choyamba sonkhanitsani udzu ndi kuumanga m’mitolo kuti ukatenthedwe, ndipo mukatha mupite kukasonkhanitsa tirigu ndi kumuika m’nkhokwe yanga.’”​—Mat. 13:24-30.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena