Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Baibulo la Dziko Latsopano Linamasuliridwa Molondola?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
    • Yesu akulalikira paphiri ndipo khamu la anthu likumvetsera

      Kugwiritsira ntchito mawu osiyanasiyana. Nthawi zambiri mavesi a m’Baibulo amene amasuliridwa liwu ndi liwu amakhala osamveka bwino. Mwachitsanzo pomasulira liwu ndi liwu mawu a Yesu a pa Mateyu 5:3, Baibulo la Buku Lopatulika Ndilo Mau a Mulungu limati: “Odala ali osauka mumzimu.” Anthu ambiri amaona kuti mawu akuti “osauka mumzimu” ndi ovuta kumvetsa ndipo ena amaganiza kuti Yesu ankanena za kufunika kokhala munthu wodzichepetsa kapena wosauka. Komatu apa Yesu ankatanthauza kuti munthu angapeze chimwemwe chenicheni ngati akutsogoleredwa ndi Mulungu. Choncho Baibulo la Dziko Latsopano linamasulira mawu a Yesu amenewa molondola, ponena kuti “anthu amene amazindikira zosowa zawo zauzimu.”​—Mateyu 5:3.c

  • Kodi Baibulo la Dziko Latsopano Linamasuliridwa Molondola?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
    • c Mofanana ndi zimenezi, Baibulo la J. B.Phillips linamasulira vesili kuti, “amene amazindikira kuti akufunikira Mulungu,” ndiponso Baibulo la The Translator’s New Testament linamasulira vesili kuti “amene amazindikira kuti akufunikira zinthu zauzimu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena