Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Mukudziwa?
    Nsanja ya Olonda—2011 | October 1
    • ▪ Yesu atatsala pang’ono kuphedwa, anathetsa zinthu zopanda chilungamo zimene zinkachitika m’kachisi. Baibulo limati: ‘Yesu anathamangitsa onse ogulitsa ndi ogula m’kachisimo, ndipo anagubuduza matebulo a osintha ndalama ndi mabenchi a ogulitsa nkhunda. Iye anawauza kuti: “Malemba amati, ‘Nyumba yanga idzatchedwa nyumba yopemphereramo,’ koma inu mukuisandutsa phanga la achifwamba.”’​—Mateyu 21:12, 13.

  • Kodi Mukudziwa?
    Nsanja ya Olonda—2011 | October 1
    • Popeza Yesu anadzudzula osintha ndalamawa kuti anasandutsa kachisi kukhala “phanga la achifwamba,” ndiye kuti iwo ankabera anthu powalipiritsa ndalama zambiri akafuna kusinthitsa ndalama zawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena