Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ulaliki Wotchuka wa Paphiri
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
    • Iye anati: “Odala ndi anthu amene amazindikira zosowa zawo zauzimu, chifukwa ufumu wakumwamba ndi wawo. Odala ndi anthu amene akumva chisoni, chifukwa adzasangalatsidwa. . . . Odala ndi anthu amene akumva njala ndi ludzu la chilungamo, chifukwa adzakhuta. . . .  Odala ndi anthu amene akuzunzidwa chifukwa cha chilungamo, pakuti ufumu wakumwamba ndi wawo. Ndinu odala pamene anthu akukunyozani ndi kukuzunzani,  . . chifukwa cha ine. Kondwerani, dumphani ndi chimwemwe.”—Mateyu 5:3-12.

  • Ulaliki Wotchuka wa Paphiri
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
    • Yesu ananena kuti anthu amene amazindikira zosowa zawo zauzimu, amene amadzimvera chisoni chifukwa chakuti ndi ochimwa komanso amene amafuna kumudziwadi Mulungu ndi kumutumikira, amenewo ndi amene amakhaladi osangalala kapena kuti odala. Akamazunzidwa kapena anthu ena akamadana nawo chifukwa chochita zimene Mulungu amafuna, amakhalabe osangalala chifukwa amadziwa kuti akuchita zinthu zosangalatsa Mulungu komanso kuti adzawadalitsa powapatsa moyo wosatha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena