-
“Mitima Yanu Isavutike”Nsanja ya Olonda—1988 | February 15
-
-
14. Ndimotani mmene tingadziŵire kaya kuchonderera kofunitsitsa kwa Yehova kufunikira kuchitidwa kamodzi kokha?
14 Chiri chofunika kudziŵa kuti kuchonderera kofunitsitsa koteroko kwa Yehova kaŵirikaŵiri sikuchitidwa kamodzi kokha. Yesu anaphunzitsa mu Ulaliki wake wotchuka wa pa Phiri: “Pitirizani kupempha, ndipo chidzapatsidwa kwa inu; pitirizani kufunafuna, ndipo mudzapeza; pitirizani kugogoda, ndipo chidzatsegulidwa kwa inu.” (Mateyu 7:7, NW) Malembedwe ambiri a Baibulo amapereka motere: “Pemphani . . . funani . . . gogodani.” Koma Chigriki choyambirira chimapereka lingaliro la kachitidwe kopitirizabe.a
-
-
“Mitima Yanu Isavutike”Nsanja ya Olonda—1988 | February 15
-
-
a M’kugwirizana ndi kulondola kwa New World Translation of the Holy Scriptures, Charles B. Williams akutembenuza versilo motere: “Pitirizani kupempha . . . pitirizani kufuna . . . pitirizani kugogoda, ndipo chitseko chidzatsegulidwa kwa inu.”—The New Testament: A Translation in the Language of the People.
-