Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nkhani ya Mwana Wotaika
    Nsanja ya Olonda—1989 | February 1
    • “Munthu wina,” Yesu akuyamba tero, “anali ndi ana amuna aŵiri. Ndipo wam’ng’onoyo anati kwa atate wake, ‘Atate, ndigawirenitu zanga za pa chuma chanu.’ Ndipo [atateyo] anagawira za moyo wake.” Kodi nchiyani chimene wam’ng’onoyo akuchita ndi zimene walandira?

  • Nkhani ya Mwana Wotaika
    Nsanja ya Olonda—1989 | February 1
    • Pano pali chinachake choyenera kulingalira: Ngati atate wake anamtembenukira iye ndi kufuula mwaukali pa iye pamene iye anachoka panyumba, mwana wamwamunayo mwachidziŵikire sakanakhoza kukhala wa malingaliro amodzi chotero ponena za chimene iye akachita. Iye akanagamulapo kubwerera ndi kuyesera kupeza ntchito kwinakwake m’dziko la kumudzi kwawo kotero kuti sakanakhoza kuyang’anizana ndi atate wake. Ngakhale kuli tero, palibe ganizo lirilonse loterolo linaloŵa m’malingaliro ake. Kumudzi ndi kumene iye anafuna kukhala!

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena