Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Baibulo Limati Chiyani pa Nkhani ya Miliri?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Kodi Baibulo linaneneratu za miliri?

      Baibulo silitchula mayina a miliri monga COVID-19, Edzi, TB, malungo kapena chimfine cha ku Spain. Koma linaneneratu kuti “kudzakhala miliri” ndi “mliri wakupha.” (Luka 21:11; Chivumbulutso 6:8) Miliri imeneyi ndi mbali ya chizindikiro cha “masiku otsiriza” omwe amatchedwanso “mapeto a nthawi ino.”—2 Timoteyo 3:1; Mateyu 24:3.

  • Kodi Baibulo Limati Chiyani pa Nkhani ya Miliri?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Luka 21:11: “Kudzakhala miliri.”

      Tanthauzo lake: Matenda amene akufalikira padziko lonse, ndi mbali ya chizindikiro cha masiku otsiriza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena