Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsamba 2
  • Muzikhala Owolowa Manja

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzikhala Owolowa Manja
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Anthu Opatsa Amakhala Osangalala
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Nsembe Yosonyeza Kuyamikira
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • “Tsopano Uona Zimene Ndichite kwa Farao”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Ubwino wa Mtima Wopatsa
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 July tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LUKA 6-7

Muzikhala Owolowa Manja

6:38

Munthu wowolowa manja amasangalala akamagwiritsa ntchito nthawi, mphamvu komanso zinthu zake pothandiza ndi kulimbikitsa ena.

  • Munthu wanyamula tirigu pa malaya ake akunja omwe wawapinda

    Mawu achigiriki omwe anawamasulira kuti “khalani opatsa” amasonyeza kukhala ndi chizolowezi chopatsa ena zinthu

  • Tikakhala opatsa, ena adzakhuthulira m’matumba athu “muyezo wabwino, wotsendereka, wokhutchumuka ndi wosefukira.” Mawu a palembali angatanthauze zimene zinkachitika ogulitsa akamakhuthulira zinthu pamalaya akunja a munthu amene akugula

M’bale wachinyamata akuthandiza m’bale wachikulire pomuperekeza kumsika

Kodi mungagwiritse ntchito malangizo amenewa pa nthawi iti?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena