Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesu Anapereka Malangizo pa Nkhani ya Chuma
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
    • Kodi ndi ndani amene ankafunika kufunafuna Ufumu wa Mulungu? Yesu ananena kuti amene azidzachita zimenezi ndi anthu ochepa okhulupirika a “kagulu ka nkhosa.” Ndipo patapita nthawi zinadzadziwika kuti chiwerengero cha anthuwo chinali 144,000. Kodi kagulu kameneka kankayembekezera chiyani? Yesu ananena kuti: “Atate wanu wavomereza kukupatsani ufumu.” Anthu a mu kaguluka saganizira kwambiri zopeza chuma cha m’dzikoli, chomwe anthu akhoza kuba, koma amaganizira za “chuma chosatha kumwamba,” komwe akalamulire ndi Khristu.—Luka 12:32-34.

  • Woyang’anira Nyumba Wokhulupirika Ayenera Kukhala Wokonzeka
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
    • Yesu anafotokoza kuti a “kagulu ka nkhosa” okha ndi amene ali ndi malo mu Ufumu wakumwamba. (Luka 12:32) Koma munthu amene wapatsidwa mwayi umenewu sayenera kuuona mopepuka. Ndipotu Yesu anafotokoza kufunika koti munthu amene wasankhidwa kuti akalamulire nawo mu Ufumu aziona zinthu moyenera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena