-
Yerusalemu ndi Kachisi Amene Yesu Ankamudziŵa‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
Zinthu zofunika zimene zinachitika Yesu asanafe, zinachitikira m’Yerusalemu kapena malo ena pafupi ndi mzindawo: m’munda wa Getsemane, kumene Yesu anapemphera; Bwalo la Akulu (Sanihedrini); m’nyumba ya Kayafa; m’nyumba ya Kazembe Pilato ndipo pomaliza ku Gologota.—Marko 14:32, 14:53–15:1, 16, 22; Yoh. 18:1, 13, 24, 28.
-
-
Yerusalemu ndi Kachisi Amene Yesu Ankamudziŵa‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
Thamanda la Siloamu
-