Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Yesu Ndi Ndani?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
    • 6. Kuphunzira zokhudza Yesu kumatithandiza kwambiri

      Baibulo limatilimbikitsa kuti tiyenera kuphunzira zokhudza Yesu komanso udindo umene Mulungu anamupatsa. Werengani Yohane 14:6 ndi 17:3, kenako mukambirane funso ili:

      • Kodi kuphunzira zokhudza Yesu n’kofunika chifukwa chiyani?

      Yesu akuphunzitsa amuna, akazi ndi ana.

      Yesu anatsegula njira yotithandiza kuti Mulungu akhale mnzathu. Iye anaphunzitsa choonadi chonena za Yehova komanso kudzera mwa Yesuyo tikhoza kudzapeza moyo wosatha

  • Kodi Yesu Ndi Ndani?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena