Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ntchito ya Alembi Akale Yokopera Mawu a Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2007 | March 15
    • Kale Alembi Analiko ku Isiraeli

      Mose anakulira m’banja la Farao. (Eksodo 2:10; Machitidwe 7:21, 22) Akatswiri a mbiri ya Iguputo wakale amati zimene Mose anaphunzira zingaphatikizepo kuwerenga ndi kulemba bwino kalembedwe ka Aiguputo komanso zina ndi zina za ntchito yaulembi. M’buku lake, pulofesa James K. Hoffmeier anati: “M’pake kukhulupirira zimene Baibulo limanena kuti Mose ankatha kulemba zochitika, maulendo, ndi zinthu zina zokhudzana ndi ntchito yaulembi.”b​—Israel in Egypt.

  • Ntchito ya Alembi Akale Yokopera Mawu a Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2007 | March 15
    • b Umboni wakuti Mose analemba nkhani zamalamulo umapezeka pa Eksodo 24:4, 7; 34:27, 28 ndi pa Deuteronomo 31:24-26. Nyimbo imene analemba imatchulidwa pa Deuteronomo 31:22, ndipo nkhani yonena za ulendo wawo m’chipululu imatchulidwa pa Numeri 33:2.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena