Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi “Makiyi a Ufumu” N’chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Nthawi zina mawu akuti “Makiyi a Ufumu,” m’Mabaibulo ena amatchedwanso “Makiyi olowera mu ufumu.” Mawuwa amatanthauza udindo wothandiza anthu kuti ‘akalowe mu ufumu wa Mulungu.’ (Mateyu 16:19;The New American Bible; Machitidwe 14:22)a Yesu anapatsa Petulo “makiyi a ufumu wakumwamba.” Zimenezi zikutanthauza kuti Petulo anapatsidwa udindo wotsegulira anthu okhulupirika mwayi wolandira mzimu woyera wa Mulungu kuti anthuwo adzathe kulowa mu Ufumu wakumwamba.

  • Kodi “Makiyi a Ufumu” N’chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • Kodi ‘kulowa mu Ufumu’ kumatanthauza chiyani?

      Anthu amene ‘amalowa mu Ufumu,’ adzalamulira limodzi ndi Yesu kumwamba. Baibulo linaneneratu kuti anthuwa adzakhala “m’mipando yachifumu” ndipo “adzakhala mafumu olamulira dziko lapansi.”​—Luka 22:29, 30; Chivumbulutso 5:9, 10.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena