Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Tetezani Ana M’Banja Lanu
    Galamukani!—2007 | October
    • “OPANDA chikondi chachibadwa.” Baibulo limanena zimenezi pofotokoza mmene anthu ambiri alili “m’masiku otsiriza” ano. (2 Timoteyo 3:1, 3, 4) Kufala kwa vuto la kuchita chipongwe ana panyumba kukutsimikizira kuti ulosi umenewu ukukwaniritsidwa. Kwenikweni, mawu a Chigiriki akuti asʹ-tor-gos, omwe m’Chichewa amati “opanda chikondi chachibadwa,” amasonyeza kusowa chikondi chimene chimayenera kukhalapo pakati pa achibale, makamaka pakati pa makolo ndi ana awo.a Ndipotu nthawi zambiri achibale ndi amene amachita ana zachipongwe zotere.

  • Tetezani Ana M’Banja Lanu
    Galamukani!—2007 | October
    • a Mabuku ena amamasulira mawu a Chigiriki chakalewa motere: “Kuumira mtima achibale.” Motero, Baibulo lina linamasulira vesi imeneyi motere: “Adzakhala . . . osowa chikondi cha pa abale awo.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena