Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mungatani Kuti Banja Lanu Likhale Losangalala?​—Mbali Yachiwiri
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
    • 4. Muziphunzitsa ana anu mwachikondi

      Kuphunzitsa mwana si ntchito yamasewera. Koma kodi Baibulo lingakuthandizeni bwanji? Werengani Yakobo 1:19, 20, kenako mukambirane mafunso awa:

      • Kodi makolo angasonyeze bwanji chikondi akamalankhula ndi ana awo?

      • N’chifukwa chiyani makolo akakwiya sayenera kulangiza ana awo pa nthawi imeneyo?a

      Bambo anyonyomala ndipo akulankhula ndi mwana wawo yemwe wanyamula mpira m’manja. Mphika wa maluwa wagwa pansi ndipo wasweka.
  • Mungatani Kuti Banja Lanu Likhale Losangalala?​—Mbali Yachiwiri
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
    • a M’Baibulo, mawu akuti “malangizo” amatanthauza kuphunzitsa, kutsogolera komanso kuthandiza munthu kuti asinthe. Koma satanthauza kuzunza kapena kuchitira munthu nkhanza.​​—Miyambo 4:1.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena