Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 116
  • Kuwala Kukuwonjezereka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuwala Kukuwonjezereka
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwala Kukuwonjezerekabe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuunika Kumkabe Kuuŵala
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova
  • N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Anasintha Zinthu Zina Zomwe Ankakhulupirira?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 116

Nyimbo 116

Kuwala Kukuwonjezereka

Losindikizidwa

(Miyambo 4:18)

1. Aneneri akale ankafuna

Kudziwa za Yesu Mesiya.

Mzimu wa M’lungu unaneneratu

Kuti adzatipulumutsa.

Nthawi yafika, akulamulira.

Umboni wake ulipo.

Kudziwa zimenezi ndi mwayi

Waukulu womwe tili nawo.

(KOLASI)

Kuwala kwa panjira yathu

Kukuwonjezerekadi.

Zomwe M’lungu akuulula

Zimatitsogoleradi.

2. Ambuye wathu wasankha kapolo.

Ndi mmene amatidyetsera.

Ndipo m’kupita kwa nthawi kuwala

Kwa cho’nadi kwawonjezeka.

Pano tikuyenda molimba mtima,

Mowala ngati masana.

Tikuthokoza Yehova chifukwa

Cho’nadi chake watipatsa.

(KOLASI)

Kuwala kwa panjira yathu

Kukuwonjezerekadi.

Zomwe M’lungu akuulula

Zimatitsogoleradi.

(Onaninso Aroma 8:22; 1 Akor. 2:10; 1 Pet. 1:12.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena