Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 102
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 102

Nyimbo 102

Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!

Losindikizidwa

(Salimo 98:1)

1. Iyi ndi nyimbo yachisangalalo

Yolemekeza M’lungu wamkulu.

Imatipatsadi chiyembekezo,

Imba nafe nyimbo ya Ufumu.

(KOLASI)

‘Lambirani M’lungu wathu,

Mwana waketu ndi mfumu!

Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu

Tamandani dzina la Mulungu.’

2. Ndi nyimboyi tilengeza Ufumu

Khristu Yesu ndi wolamulira.

Ndipo mtundu watsopano wabadwa

Nawo ukumusangalalira.

(KOLASI)

‘Lambirani M’lungu wathu,

Mwana waketu ndi mfumu!

Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu

Tamandani dzina la Mulungu.’

3. Nyimboyi omwe angaiphunzire

Ndi amene amadzichepetsa.

M’dziko lonse ambiri aphunzira.

Akuitananso anthu ena.

(KOLASI)

‘Lambirani M’lungu wathu,

Mwana waketu ndi mfumu!

Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu

Tamandani dzina la Mulungu.’

(Onaninso Sal. 95:6; 1 Pet. 2:9, 10; Chiv. 12:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena