Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 121
  • Tizilimbikitsana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizilimbikitsana
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tizilimbikitsana
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Pitirizani Kutonthozana ndi Kulimbikitsana”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Mungachite Kuti Mulungu Apitirize Kukukondani
    Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?
  • Fulumizanani ku Chikondano ndi Ntchito Zabwino—MotanI?
    Nsanja ya Olonda—1995
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 121

Nyimbo 121

Tizilimbikitsana

Losindikizidwa

(Aheberi 10:24, 25)

1. Pomwe timalimbikitsana

Kutumikira Yehova

Timakhaladi okondana

Komanso ogwirizana.

Chikondi cha anthu a M’lungu

Chimatipatsadi mphamvu.

Kumene tingatetezeke

Ndi mkati mwa mpingo wathu.

2. Mawu ochoka kwa abale

A pa nthawi yoyenera

Ndi olimbikitsa kwambiri

Ndipo amatitonthoza.

Kugwirira ntchito limodzi

Ndithu ndikosangalatsa,

Timafuna kuthandizana

Ndi kumalimbikitsana.

3. Popeza tsiku la Yehova

Layandikira kwambiri

Ndikofunika tisaleke

Kusonkhanatu pamodzi.

Tikufuna kutumikira

Ndi abale kwamuyaya.

Choncho ndi njira yachikondi

Kuti tizithandizana.

(Onaninso Luka 22:32; Mac. 14:21, 22; Agal. 6:2; 1 Ates. 5:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena