Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 45
  • Pitani Patsogolo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitani Patsogolo
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Pita Patsogolo
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitani Patsogolo!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Muzionetsa Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 45

Nyimbo 45

Pitani Patsogolo

Losindikizidwa

(Aheberi 6:1)

1. Pita patsogolo kula mu mzimu!

Mulungu afuna tikhaledi aluso.

Sonyezatu luso muutumiki,

M’lungu adzadalitsa.

Utumikiwu ndi wa onse.

Yesu naye anauchita.

Dalira Mulungu kuti usagwe,

Limba pa chilungamo.

2. Pita patsogolo molimba mtima!

Lalika uthenga kwa anthu onse m’dziko.

Tamanda Yehova Mfumu yathuyo,

Polalikira nawo.

Adani angatiopseze.

Tisaleke, onse amvetu

Kuti Ufumu wa M’lungu wayamba.

Phunzitsa choonadi.

3. Pita patsogolo usabwerere,

Wonjezera luso ntchitoyi n’njaikulu.

Mzimu wa Mulungu ukuthandize,

Udzapeza chimwemwe.

Konda anthu omwe wapeza.

Bwerera, uwafike m’mtima.

Athandize apite patsogolo,

Cho’nadi chiziwala.

(Onaninso Afil. 1:27; 3:16; Aheb. 10:39.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena