Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 11
  • Tikondweretse Mtima wa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikondweretse Mtima wa Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tizisangalatsa Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukondweretsa Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ana Amene Amakondwereta Mtima wa Yehova
    Nsanja ya Olonda—1987
  • ‘Kondwerani, Anthu Inu’!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 11

Nyimbo 11

Tikondweretse Mtima wa Yehova

Losindikizidwa

(Miyambo 27:11)

1. M’lungu takulonjezani,

kuchita zofuna zanu.

Tidzagwira ntchito yanu

Mtima wanu ukondwere.

2. Kapolo wanu padziko,

Amapereka chakudya

Iye amatithandiza

Kuchita zofuna zanu.

3. Mutipatse mzimu wanu,

Kuti tikhulupirike

Inde tikutamandeni,

Mtima wanu ukondwere.

(Onaninso Mat. 24:45-47; Luka 11:13; 22:42.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena