Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 64
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikonda Kwambiri Choonadi Panokha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 64

Nyimbo 64

Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi

Losindikizidwa

(Miyambo 3:1, 2)

1. Njira yabwino ndiyo ya choonadi

Wina sangakusankhireni.

Choncho malangizo a M’lungu mverani,

Ndipo m’khulupilireni.

(KOLASI)

M’konde cho’nadi,

Chikhale chanuchanu.

Ndipo mudzakhala

Achimwemwe

Mukakonda cho’nadi.

2. Mukatumikira Mulungu mwakhama

Mudzalandira madalitso,

Komanso mudzapeza moyo wosatha,

Wamtendere ndi wabwino.

(KOLASI)

M’konde cho’nadi,

Chikhale chanuchanu.

Ndipo mudzakhala

Achimwemwe

Mukakonda cho’nadi.

3. M’maso mwa M’lungu tilitu ngati ana

Ofunika kulangizidwa.

Tiyende naye Atate wakumwamba,

Choncho tidzadalitsidwa.

(KOLASI)

M’konde cho’nadi,

Chikhale chanuchanu.

Ndipo mudzakhala

Achimwemwe

Mukakonda cho’nadi.

(Onaninso Sal. 26:3; Miy. 8:35; 15:31; Yoh. 8:31, 32.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena