Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 132
  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Dzina la Atate Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 132

Nyimbo 132

Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana

Losindikizidwa

(Ekisodo 15:1)

1. Muimbireni Yehova M’lungu wokwezeka.

Anaponya m’nyanja Aigup’to onyada.

Tamandani Ya. Palibe wina womuposa.

Yehova ndi dzina lake. Ndi wopambana.

(KOLASI)

Yehova ndinu wokwezeka

Simunasinthe ndinube Mfumu.

Adani anu muwagonjetsa

N’kuyeretsa dzina lanu.

2. Mitundu yonse eti ikutsutsa Yehova.

Iwonongedwabe ngakhale ndi yamphamvu.

Posachedwapa isesedwa ndi Amagedo.

Idzadziwa kuti Yehova ndi Mulungu.

(KOLASI)

Yehova ndinu wokwezeka

Simunasinthe ndinube Mfumu.

Adani anu muwagonjetsa

N’kuyeretsa dzina lanu.

(Onaninso Sal. 2:2, 9; 92:8; Mal. 3:6; Chiv. 16:16.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena