Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 147
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 147

NYIMBO 147

Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha

Losindikizidwa

(Salimo 37:29)

  1. 1. Mulungu watilonjeza

    Moyo womwe sudzatha.

    Anthu adzasangalala,

    Zidzachitikadi.

    (KOLASI)

    Inde tidzakhala

    Ndi moyo wosatha.

    M’lungu walonjeza

    Zidzachitika.

  2. 2. Mudziko latsopanolo

    Uchimowu udzatha.

    Mudzakhaladi mtendere

    Wochoka kwa M’lungu.

    (KOLASI)

    Inde tidzakhala

    Ndi moyo wosatha.

    M’lungu walonjeza

    Zidzachitika.

  3. 3. Akufawo adzauka,

    Chisoninso chidzatha.

    Mulungu adzapukuta

    Misozi ya anthu.

    (KOLASI)

    Inde tidzakhala

    Ndi moyo wosatha.

    M’lungu walonjeza

    Zidzachitika.

(Onaninso Yes. 25:8; Luka 23:43; Yoh. 11:25; Chiv. 21:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena