Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 141
  • Moyo Ndi Wodabwitsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo Ndi Wodabwitsa
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 141

NYIMBO 141

Moyo Ndi Wodabwitsa

Losindikizidwa

(Salimo 36:9)

  1. 1. Mphatso ya moyo ndiponso mvula,

    Mbewu komanso kuwala kwa dzuwa,

    Mulungu ndiye amatipatsa

    Mphatsozi ndipo zimatithandizadi.

    (KOLASI)

    Tingachite chani ndi mphatso iyi?

    Tizikonda M’lungu yemwe anatipatsa.

    Sitingaipeze mphatsoyi patokha,

    Mphatso yaketu ndi moyo wodabwitsa.

  2. 2. Ena potopa ndi mavutowa

    Angamanene kuti bola kufa.

    Koma ifeyo sitili choncho.

    Timathokoza kuti tili ndi moyo.

    (KOLASI)

    Tingachite chani ndi mphatso iyi?

    Tizikonda anzathu omwe tili nawo.

    Sitingaipeze mphatsoyi patokha,

    Mphatso yaketu ndi moyo wodabwitsa.

(Onaninso Yobu 2:9; Sal. 34:12; Mlal. 8:15; Mat. 22:​37-40; Aroma 6:23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena