Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 64
  • Tizigwira Ntchito Yokolola Mosangalala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizigwira Ntchito Yokolola Mosangalala
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tigwire Ntchito Yokolola Mosangalala
    Imbirani Yehova
  • Kugaŵana Mokondwa m’Kututa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 64

NYIMBO 64

Tizigwira Ntchito Yokolola Mosangalala

Losindikizidwa

(Mateyu 13:​1-23)

  1. 1 .Tili munthawi yokolola,

    Ndi nthawidi yapadera.

    M’mundamo tirigu wachamo

    Tiyeni tikakolole.

    Yesu akutitsogolera,

    Ndi chitsanzodi chabwino.

    Ndi mwayi wapadera kwambiri

    Kugwira nawo ntchitoyi.

  2. 2. Timakonda M’lungu ndi anthu

    Choncho timachita khama.

    Tiphunzitse anthu mwachangu,

    Mapeto ayandikira.

    Yehova amatidalitsa,

    Timakhala ndi chimwemwe.

    Tipirire pogwira ntchitoyi

    M’lungu adzatithandiza.

(Onaninso Mat. 24:13; 1 Akor. 3:9; 2 Tim. 4:2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena