-
Kuloŵa Mmalo KwautumwiKukambitsirana za m’Malemba
-
-
mnzake; osafanana ndi Kaini, amene anali wa Woipayo nadula pakhosi mbale wake.”
Mounikiridwa ndi zapamwambapazi, kodi awo odzinenera kukhala oloŵa mmalo atumwi aphunzitsadi ndi kuchita zimene Kristu ndi Atumwi ake anachita?
-
-
KumwambaKukambitsirana za m’Malemba
-
-
Kumwamba
Tanthauzo: Malo okhala Yehova Mulungu ndi zolengedwa zauzimu zokhulupirika; chigawo chosawoneka ndi maso aumunthu. Baibulo limagwiritsiranso ntchito liwu lakuti “kumwamba” m’malingaliro ena osiyanasiyana; mwachitsanzo: Kuimira Mulungu mwiniyo, gulu lake la zolengedwa zauzimu zokhulupirika, malo a chiyanjo cha Mulungu, chilengedwe chakuthupi chosaphatikizapo dziko lapansi, m’mlengalenga mozungulira planetili Dziko Lapansi, maboma aumunthu otsogozedwa ndi Satana, ndi boma latsopano lolungama lakumwamba m’limene Yesu Kristu limodzi ndi oloŵa nyumba anzake apatsidwa mphamvu ndi Yehova kulamulira.
Kodi tonsefe tinayamba takhala m’chigawo chamizimu tisanabadwe monga anthu?
Yoh. 8:23: “[Yesu Kristu anati] Inu ndinu ochokera pansi; ine ndine wochokera kumwamba; inu ndinu a m’dziko lino lapansi; sindiri ine wa dziko lino lapansi.” (Yesu anachokera ku malo a mizimu. Koma monga momwe Yesu adanenera, anthu anewo sanatero.)
Aroma 9:10-12: “Rebeka anakhala ndi pakati pa amapasa . . . asanabadwe, kapena asanachite kanthu kabwino kapena koipa, kuti kutsimikiza mtima kwa Mulungu monga mwa kusankha kukhale, sichifukwa cha ntchito ayi, koma chifukwa cha wakuitananiyo, chotero kunanenedwa kwa uyo, Wamkulu adzakhala kapolo wa wamng’ono.” (Ndithudi, ngati amapasa Yakobo ndi Esau anali atakhala ndi moyo kalelo m’malo a mizimu iwo akanakhaladi ndi cholembedwa chozikidwa pamkhalidwe wawo kumeneko, kodi sichoncho? Koma analibe cholembedwa chotero kufikira pambuyo pa kubadwa kwawo monga anthu.)
Kodi anthu onse abwino amapita kumwamba?
Mac. 2:34: “Davide [amene Baibulo limamtchula kukhala
-