Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 23
  • Chiyembekezo Chabaibulo cha Mtundu wa Anthu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chiyembekezo Chabaibulo cha Mtundu wa Anthu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • “Mulungu Akhale Wowona”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 23

Nyimbo 23

Chiyembekezo Chabaibulo cha Mtundu wa Anthu

(Aroma 12:12)

1. Tsiku ladza; lowopsadi

Anthu ayembekeza motaya mtima.

Samawona, adzandira

Pamene dziko litha.

Koma m’Baibulo muli chifukwa

Chosangalalira Ufumu wadza.

Ya adzapukuta misozi yonse.

Tukulani mitu; musawopetu.

2. Moyowutu ngwamavuto,

Onse sangakane, anthu amafadi.

Sangapeŵe manda konse;

Ntchito zawo nzachabe.

Koma Baibulo liri nachotu

Chiyembekezo cha chiukiliro.

Anthu adzamka kumadzi a moyo.

Mbiriyi yanenedwa ndi Yehova.

3. Amanyoza Mulunguyo

Namtsutsa mwamwano, nayenda m’zoipa.

Satanayo alamula;

Kuipa kuli ponse.

Koma Baibulo limatiuza

Kuti Yehova adzaweruzadi,

Oipa adzachotsedwa kosatha,

Koma ofatsa adzadzaza dziko.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena