Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ba tsamba 32
  • Chikuto Chakumbuyo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikuto Chakumbuyo
  • Buku la Anthu Onse
Buku la Anthu Onse
ba tsamba 32

Chikuto Chakumbuyo

Kodi ndi Buku Lina Liti

• limene lasonkhezera kwambiri maluso abwino kwambiri padziko lapansi ojambula, olemba mabuku, ndi a nyimbo, limenenso lakhudza kwambiri zamalamulo?

• limene lapulumuka zaka zikwi zambiri za kukopedwa pamanja komanso lafika kwa ife monga momwedi linalembedwera?

• limene lasonkhezera ena kukhala ndi mzimu wopanda dyera kwakuti akhala okonzeka kuvutika ngakhale kufa kuti alitembenuze?

• limene latembenuzidwa m’zinenero zoposa 2,100, likumapezeka kwa oposa 90 peresenti ya anthu onse padziko lapansi?

• limene limatchula zenizeni za sayansi zimene anthu anadzazitulukira pambuyo pake patapita zaka mazana ambiri?

• limene lili ndi mfundo zosasintha ndi nthaŵi zimene zingathandize anthu a fuko, mtundu, ndi dziko lililonse kuwongolera moyo wawo?

• limene lili ndi maulosi olondola amene anakwaniritsidwa, monga momwe mbiri ikusonyezera?

Kodi sikungakhale koyenera kulipenda buku limenelo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena