Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 173
  • Chikondi—Chomangira Champhumphu cha Umodzi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikondi—Chomangira Champhumphu cha Umodzi
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kulani M’chikondi
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Kodi Tingatani Kuti Tizikondana Kwambiri?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
  • Kodi Chikondi Chanu N’chosefukira Motani?
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 173

Nyimbo 173

Chikondi—Chomangira Champhumphu cha Umodzi

(Akolose 3:14)

1. Chikondicho chazirala

M’nthaŵi yamapeto.

Ife tisunge chikondi

Popeŵa kutero.

Tikatsanzira Mulungu,

Tidzapatsa onse

Chikondi cha Mulunguyo

Chochoka mumtima.

2. Chikondi chosanyengeza,

Chikondi chakuya,

Tiyeni tichikulitse

Ndi kuchipereka.

Tiyeni tifike mtima

Wa abale athu.

Okondedwa ndi Mulungu

Ife tiwakonde.

3. Dongosololi likugwa

Tikhale amodzi.

Chomangira cha umodzi

Tichigwiritsitse.

Chikondi chenichenidi

Chiri chofunika.

Chidzatidzetsa pafupi,

Mpaka ntchito itha.

4. Unansi wabwino ndi Ya

Udzatithandiza

Kukonda ena monga ’fe

Munthaŵi yovuta.

Chikondi chathu chilimbe

Mukuwona mtima.

Chomangira cha umodzi

Chikondi chitero.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena