Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 110
  • Khalani Wokhululukira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Wokhululukira
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikhululuka
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Muzikhululuka
    Imbirani Yehova
  • “Yehova Anakukhululukirani ndi Mtima Wonse”
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Yehova Ndi Wokhulupirika Ndiponso Amakhululuka
    Nsanja ya Olonda—2013
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 110

Nyimbo 110

Khalani Wokhululukira

(Aefeso 4:32)

1. Mwachikondi M’lungu wathu,

Napanga makonzedwe,

Natumiza Mwana wake,

Chithandizo napatsa.

Pamene ife tilapa,

Akhululukiradi

Mwachiwombolo cha Kristu,

Tipemphatu chifundo.

2. M’lungu akhululukira

Yemwe amutsanzira,

Nakhululukira ena,

Kusonyeza chifundo.

Poti ife siangwiro,

Tilakwa nthaŵi zonse

Pa zirizonse zoipa.

Tikhululukireni.

3. Ndithu masiku ngoipa

Tikhululukiretu;

Chikondi tisonyezebe

Nzeru yodzera m’mwamba.

Kukhululukira ena

Uchikulire ngwathu,

Mwachidziŵitso chakuya

Tisungetu mtendere.

4. Kukhululuka kowona

Ife tikukulitse.

Kudzatithandizatunso,

Kuthetsa makaniwo.

Pamene tikhululuka,

Tifanana ndi M’lungu,

Wokonda kukhululuka,

Atama chisomocho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena