Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 127
  • Unyinji wa Abale

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Unyinji wa Abale
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Abale Ambirimbiri
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khamu la Abale
    Imbirani Yehova
  • Tsoka Lachiwiri Linali Makamu a Asilikali Okwera Pamahatchi
    Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
  • Zimene Muyenera Kudziwa Zokhudza Angelo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 127

Nyimbo 127

Unyinji wa Abale

(Chivumbulutso 7:9)

1. Abale m’yanda miyanda

Aima ndi ine

Mboni zodalirika,

Zosunga umphumphu.

Miyanda miyandadi,

Khamu lamphamvudi.

M’mitundu yonse padziko

Atamanda M’lungu.

2. Abale m’yanda miyanda,

Ovala zoyera,

Ali m’kachisi wa Ya,

’Sana ndi usiku.

Miyanda miyandadi.

Adziŵitsa anthu

Kuti chipulumutsocho

Chiri kwa Yehova.

3. Abale m’yanda miyanda

—Alalika ‘mbiri

Yabwinoyo yosatha,’

Anthu onse amve.

Amalalikirabe,

Nkana apsinjidwa,

Kristu awatsogolera,

Apeza mtendere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena