Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 2
  • Kumvera Mulungu Koposa Anthu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kumvera Mulungu Koposa Anthu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kodi Tiyenera Kukhala Mtundu Wanji wa Anthu?
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 2

Nyimbo 2

Kumvera Mulungu Koposa Anthu

(Machitidwe 5:29)

1. Tikondweretsa Mulungu;

Tinasiya dziko.

Anthu oipa atida,

Koma sitileka.

Tifuna kumvera M’lungu

Koposa anthuwo.

Timachita zinthu zonse

Modalira Iye.

2. Za “Kaisara” timpatsa,

Ndi olamulira.

Kwa Yehova mkhalidwewo

Usonya ulemu.

Koma poti tinagudwa

Sitiri a ife,

Tikumbuka malangizo

Kutumikira Ya.

3. Tikatamatu Yehova

Mtendere ndiwathu,

Tisayende muuchi mo

Kape na mundewu.

Timatumikira M’lungu,

Ndi kumpatsa zake,

Mosawopa tiri mboni

Za Ufumu wake.

4. Ntchito yathu imayamba.

Sitidzathupsidwa,

Poti ambiri ngaludzu;

Alaŵetu Mawu.

Ena akadodometsa,

Tidziŵa zochita:

Kumvera Mulungu wathu;

Sadzatisiyatu!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena