Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 115
  • ‘Kondananidi’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Kondananidi’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Koposa Zonse Mukhale Nacho Chikondano Chenicheni”
    Dikirani!
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
  • Khalani Ndi Chikondi Chimene Sichitha Konse
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kulani M’chikondi
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 115

Nyimbo 115

‘Kondananidi’

(1 Petro 4:8)

1. Chikondi chachikulu

Chiri cha chipiliro

Chipezetsa chiyanjo,

Potumikira.

M’lungu anatumiza

Yesuyo Bwenzi lathu,

Kudzakonza unansi

Tikhale naye.

Ife owopa M’lungu

Tikhale ndi chikondi,

Poyenda mwa Kristudi,

Kukondanadi.

M’dziko la udanili

Tisonyeze chikondi.

Tilondole njirayo—

Kutsanzira Ya, Kutsanzira Ya.

2. Chikondi chosanyenga

Sichikhumudwitsidwa,

Chisonyeza ulemu

Kwa abalewo.

Chiri choleza mtima,

Sichiri chathu chokha,

Chifulatira zonse

Kwa owopa Ya.

Mapeto ayandika,

O tizindikiretu

Chikondicho chikule

Kwa anthu onse!

Tiyeni tikondane

Ndi nzeru yakumwamba.

Titsanzire Mulungu

Kunthaŵi zonse, Kunthaŵi zonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena