Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 108
  • Mawu a Yehova Ngokhulupirika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu a Yehova Ngokhulupirika
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Iye Amafuna Kuti Zinthu Zizitiyendera Bwino
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Zimene Yoswa Anakumbukira
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Yoswa
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Amakwaniritsa Malonjezo
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 108

Nyimbo 108

Mawu a Yehova Ngokhulupirika

(Yoswa 23:14)

1. Monga mvula yochoka kumwamba

Ichititsa zinthu kumera,

Mofananadi ndi mawu a Ya;

Adzapambana ndi kuwoneka.

2. Yoswa anauza Israyeli

Za ubwino wa Ya kwa iwo.

Zinthu zolonjezedwa ndi M’lungu

Zinachitika; kusonya mphavu.

3. Ya anati kwa olonjezedwa

Mawu ake ali owona.

‘Ndilumbira ndithu’ atero Ya.

Zitipatsa chiyembekezodi.

4. Tingatsimikize m’mawu Ake.

Lonjezo lake lipambana.

Akukonza Dongosolo lina,

Tidzamutamandabe Yehova.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena