Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 117
  • Ukwati—Makonzedwe a Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ukwati—Makonzedwe a Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Pambuyo pa Tsiku la Ukwati
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
  • Ukwati Ndi Mphatso Yochokera Kwa Mulungu Wachikondi
    Kodi Mungatani Kuti ‘Mulungu Apitirize Kukukondani’?
  • Ukwati Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
  • Khalanibe ndi “Chingwe cha Nkhosi Zitatu” M’banja Lanu
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 117

Nyimbo 117

Ukwati—Makonzedwe a Mulungu

(Mateyu 19:4-6)

1. Ukwati ngwa Mulungu.

Anauyambitsa.

Umaumba umodzi,

Udzetsa dalitso.

Goli lomangilira

Mwamuna ndi mkazi

Adzalambira M’lungu

—Yense ndi mnzakedi.

2. M’lungu ali ndi bukhu

La ’phungu wanzeru.

Linena za umutu,

Wa amuna onse.

‘Mkondeni monga mwini.’

Mulungu afuna.

Wochitira ulemu

Ali ngati ngale.

3. Nkhosi ziri zolimba

Ziposa ziŵiri.

Ya ’kakhala mu’kwati,

mavuto achepa.

Kupatsa nkwabwinodi.

Cho’nadi tidziŵa.

Choncho Pomtumikira,

Tipereke ndithu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena