Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 73
  • “Nzeru Iri ndi Odzichepetsa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Nzeru Iri ndi Odzichepetsa”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kudzichepetsa N’kofunika Kwambiri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kodi Tingatani Kuti Nthawi Zonse Tizikhala Odzichepetsa?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • “Nzeru Ili Ndi Odzichepetsa”
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Kudzichepetsa—Mkhalidwe Umene Umalimbikitsa Mtendere
    Nsanja ya Olonda—2000
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 73

Nyimbo 73

“Nzeru Iri ndi Odzichepetsa”

(Miyambo 11:2)

1. Tikayenda ndi Mulungu,

Tifune kudzichepetsa,

Kudziŵa ukulu wa Ya

Ndi kuchepetsetsa kwathu!

2. Tiri ‘akapolo chabe’!

Timavomereza izi.

Ngatitu tidzichepetsa,

Tidzapindula kwambiri!

3. ‘Tiyende monga a’ng’ono,’

Anatero Mbuye wathu.

Tikakhala odzikuza,

Tilephera malangizo.

4. Titumikire mwa mantha,

Chifukwa timakonda Ya.

Kuyenda modzichepetsa

Ndiyo nzeru yakumwamba.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena