Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 132
  • Tetezerani Mtima Wanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tetezerani Mtima Wanu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tetezani Mtima Wanu
    Imbirani Yehova
  • Tiyenera Kukhala Maso Kuti Tizipewa Mayesero
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Titeteze Mtima Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Mtendere Ukhale Ndi Inu”
    Nsanja ya Olonda—1988
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 132

Nyimbo 132

Tetezerani Mtima Wanu

(Miyambo 4:23)

1. Tetezani mitima’nu,

Mudzapeza moyo.

Landirani Mawu ake

Mukudziŵa kuti

Zochita zathu ziyamba

Ndi kuganizira.

Tetezera maganizo,

Moyenera Kristu.

2. M’lungu apatsa thandizo

Kuteteza mtima.

Fikani ndi chitamando,

Mudzasamalidwa.

Phunziro la Mawu

Ake Lidzatithandiza

Ndi kuyanjana ndi onse

Oyenda m’kuŵala.

3. Sunganibe maganizo

Pazinthu zowona,

Pazoyera ndi zokoma,

Ndi zoyamikika.

Mudzakhala ndi mtendere

Polingalirabe,

Mtima wotetezeredwa

Udikira moyo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena