Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 59
  • Kuyamikira Zikumbutso za Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuyamikira Zikumbutso za Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Zikumbutso za Yehova Mumazikonda Kwambiri?
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Kodi Zikumbutso za Yehova Zikutitsitsimutsa Mwauzimu?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1995
  • Zikumbutso za Yehova Ndi Zodalirika
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Muzitsatira Lamulo la Kukoma Mtima Polankhula
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 59

Nyimbo 59

Kuyamikira Zikumbutso za Mulungu

(Salmo 119)

1. Achimwemwe ndiomvera M’lungu,

Amfuna ndi mtima wonse,

Amamvera msanga malamulo

Samasiya zilangizo.

Akondwa ndi malamulowo,

Nasimba za chifundo chake.

Amakonda malamulo ake,

Ndi kuyembekeza M’lungu.

2. Chifundo cha M’lungu nchodabwitsa;

Chipitirira miyamba!

Chiweruzo chake chitisunga,

Nkana atinamizira.

Okonda lamulo la M’lungu;

Madalitso awo sadzatha.

Monga wofunkha asangalala,

Tisangalale mu Mawu.

3. Pempho lathu limke kwa

Yehova Kuti timvetse mawuwo.

Amve pemphero ndi kutiyanja

Natipulumutse ife.

Tikhale owona kwa M’lungu,

Ndi kuchita zonena zake.

Yehova Mulungu wolungama.

Amatilimbikitsatu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena