Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 11
  • Otsalira a Asulami

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Otsalira a Asulami
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chikondi Chowona Chiri Chachipambano!
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Chitsanzo Chabwino—Msulami
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Mfundo Zazikulu za Nyimbo ya Solomo
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Msulami Ndi Chitsanzo Chabwino Kwambiri kwa Atumiki a Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 11

Nyimbo 11

Otsalira a Asulami

(Nyimbo ya Solomo 6:13)

1. “Msulami wokongola ndi wabwino,

Ubwino wauzimu ndi wambiri.

Kulankhula kwako nkokondweretsa.

Chiyanjano chako, chikundigwira.”

2. Atero mbusa wake, Kristu Yesu,

Afuna kugaŵana naye mphotho.

Ndimotani wolimba ngati khoma,

Akuyankhira kwa ’mbuye wakeyo?

3. “Kudzipereka sikungagulidwe

Chikondi chifanana ndi malaŵi.

Chikondi chowona sichimagonja.

Chikondi chako nchonga laŵi la Ya.”

4. “Otsalira” Msulami, usagonje.

Khala woyera kwa mwamuna wako.

Atsamwali ako a unamwali

Akondwa ndi mphotho udzapezayo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena