Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 139
  • Mvetserani Mbiri ya Ufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mvetserani Mbiri ya Ufumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mtundu Woyera wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imani ndi Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Thaŵirani ku Ufumu wa Mulungu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova, Nyonga Yathu ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 139

Nyimbo 139

Mvetserani Mbiri ya Ufumu

(Yesaya 55:7)

1. Mvetserani Mbiri ya Ufumu lero

Yesu akuti: ‘Ndilamulira.

Posachedwa otsutsa adzachotsedwa;

Chotero thaŵani musachedwe konse.’

(Korasi)

2. Mwa mboni zake Yehova aitana:

‘Inu ofatsa, Sangalalani.

Posachedwa Kristu Awonetsa mphamvu

Pamene zovuta zonse zidzachoka.’

(Korasi)

3. Achimwemwe ndi anthu akumva lero

Ndi kumanena: ‘M’lungu ndimvera.’

M’lungu awasunga okhulupirika,

Omafuna choyamba Ufumu wake.

(KORASi)

Kwa oipa tinene alape,

Asandulize maganizo awo.

Aloleni apite kwa M’lungu

Ndipo adzakhululukira.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena